From the recording Imvani Pemphero Langa

In cart Not available Out of stock

This song is a direct translation of Psalm 39:12-13 which is a prayer of King David. It's sung in Chichewa. Written and composed way back in 1998 it has been an inspiration to me and our first born son in particular, who started singing it when he was just learning to speak.

Lyrics

Imvani pemphero langa Yehova
Ndipo tcherani khutu kulira kwanga
Musakhale chete pamisozi yanga
Pakuti ine ndine mlendo ndi Inu
Wosakhazikika
Monga makolo anga onse

Ndiloleni kuti nditsitsimuke
Ndisanamuke ndikukhala kuli zii
Ndiloleni kuti nditsitsimuke
Ndisanamuke ndikukhala kuli zii

22-27 January 1998